Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Genesis 34:28 - Buku Lopatulika

28 Ndipo analanda nkhosa zao ndi zoweta zao ndi abulu ao, ndi za m'mzinda, ndi za m'munda;

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

28 Ndipo analanda nkhosa zao ndi zoweta zao ndi abulu ao, ndi za m'mudzi, ndi za m'munda;

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

28 Adalanda nkhosa, zoŵeta, pamodzi ndi abulu ao ndi zonse zimene zinali mumzindamo ndiponso za ku minda yao.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

28 Analanda nkhosa zawo, ngʼombe zawo, abulu awo ndi china chilichonse chawo mu mzindamo pamodzi ndi za ku minda.

Onani mutuwo Koperani




Genesis 34:28
6 Mawu Ofanana  

Ndipo ana aamuna a Yakobo anadza kwa ophedwa nafunkha mzinda chifukwa anamuipitsa mlongo wao.


ndi chuma chao chonse ndi ana ao ndi akazi ao anawagwira, nafunkha zonse za m'nyumba.


kuti kufuula kokondwera kwa woipa sikukhalira kutha, ndi chimwemwe cha wonyoza Mulungu chikhala kamphindi?


Ndipo tsono iphani amuna onse mwa anawo, iphaninso akazi onse akudziwa mwamuna mogona naye.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa