Genesis 34:27 - Buku Lopatulika27 Ndipo ana aamuna a Yakobo anadza kwa ophedwa nafunkha mzinda chifukwa anamuipitsa mlongo wao. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201427 Ndipo ana amuna a Yakobo anadza kwa ophedwa nafunkha mudzi chifukwa anamuipitsa mlongo wao. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa27 Ana ena a Yakobe adafika pa ophedwa aja nafunkha zonse zamumzindamo, chifukwa choti anali atamgwiririra mlongo wao. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero27 Ana a Yakobo anafika kwa anthu ophedwawo ndi kututa katundu mu mzindawo chifukwa anagwiririra mlongo wawo. Onani mutuwo |