Genesis 34:26 - Buku Lopatulika26 Ndipo anapha Hamori ndi Sekemu mwana wake ndi lupanga, natulutsa Dina m'nyumba ya Sekemu nachoka naye. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201426 Ndipo anapha Hamori ndi Sekemu mwana wake ndi lupanga, natulutsa Dina m'nyumba ya Sekemu nachoka naye. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa26 Adapha Hamori ndi mwana wake Sekemu. Adamtenga Dina kumchotsa m'nyumba mwa Sekemu, nachokapo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero26 Anapha Hamori ndi Sekemu. Anakatenga Dina ku nyumba kwa Sekemu nanyamuka. Onani mutuwo |