Genesis 34:20 - Buku Lopatulika20 Ndipo Hamori ndi Sekemu mwana wake anafika ku chipata cha mzinda wao, nalankhulana ndi anthu a mzinda wao, kuti, Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201420 Ndipo Hamori ndi Sekemu mwana wake anafika ku chipata cha mudzi wao, nalankhulana ndi anthu a mudzi wao, kuti, Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa20 Tsono Hamori pamodzi ndi mwana wake Sekemu adakachita msonkhano ku chipata cha mzinda wao, nalankhula ndi anthu a m'mudzi mwao kuti, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero20 Choncho Hamori ndi mwana wake Sekemu anapita ku chipata cha mzinda wawo kukayankhula ndi anthu a mu mzindawo. Onani mutuwo |