Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Genesis 33:20 - Buku Lopatulika

20 Ndipo anamanga pamenepo guwa la nsembe, natcha pamenepo El-Elohe-Israele.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

20 Ndipo anamanga pamenepo guwa la nsembe, natcha pamenepo El-Elohe-Israele.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

20 Adamanga guwa pomwepo, nalitcha El-Elohe-Israele, ndiye kuti Mulungu, Mulungu wa Israele.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

20 Pamalopo anamanganso guwa lansembe, nalitcha Eli Elohe Israeli.

Onani mutuwo Koperani




Genesis 33:20
10 Mawu Ofanana  

Ndipo Abramu anasuntha hema wake nafika nakhala pa mitengo yathundu ya pa Mamure, imene ili mu Hebroni, nammangira Yehova kumeneko guwa la nsembe.


Ndipo Abrahamu anaoka mtengo wa bwemba pa Beereseba, naitanira pamenepo dzina la Yehova, Mulungu wa nthawi zonse.


Ndipo anati, Dzina lako silidzatchedwanso Yakobo, koma Israele, chifukwa unayesana naye Mulungu ndithu, ndipo unapambana.


Ndipo anagula ndi ndalama zana limodzi dera la munda kumeneko anamanga hema wake, padzanja la ana ake a Hamori atate wake wa Sekemu.


Ndipo Dina mwana wamkazi wa Leya, amene anambalira Yakobo, ananka kukaona akazi a kumeneko.


Ndipo anamanga kumeneko guwa la nsembe, natcha pamenepo El Betele: pakuti kumeneko Mulungu anaonekera kwa iye muja anathawa pa nkhope ya mbale wake.


Ndipo Nowa anamanga guwa la nsembe la Yehova; natengapo nyama zodyedwa zonse ndi mbalame zodyedwa zonse napereka nsembe zopsereza paguwapo.


Motero Davide analemekeza Yehova pamaso pa khamu lonse, nati Davide, Wolemekezedwa Inu, Yehova Mulungu wa Israele, Atate wathu ku nthawi zomka muyaya.


Makolo athu analambira m'phiri ili; ndipo inu munena, kuti mu Yerusalemu muli malo oyenera kulambiramo anthu.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa