Genesis 33:14 - Buku Lopatulika14 Mbuyanga atsogoleretu kapolo wake, ndipo ine ndidzazitsogolera pang'onopang'ono monga mwa mayendedwe a zoweta zili pamaso panga, ndi monga mwa mayendedwe a ana, mpaka ndifike kwa mbuyanga ku Seiri. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201414 Mbuyanga atsogoleretu kapolo wake, ndipo ine ndidzazitsogolera pang'onopang'ono monga mwa mayendedwe a zoweta zili pamaso panga, ndi monga mwa mayendedwe a ana, mpaka ndifike kwa mbuyanga ku Seiri. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa14 Chonde mbuyanga, tsogolaniko, ine ndiziyenda pang'onopang'ono pambuyo pa zoŵeta ndi ana anga, mpaka ndikakupezani ku Seiri.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero14 Choncho, mbuye wanga lolani kuti mutsogole. Ine ndiziyenda pangʼonopangʼono pambuyo pa ziwetozi ndi anawa mpaka ndikafika ku Seiri.” Onani mutuwo |