Genesis 31:49 - Buku Lopatulika49 ndi Mizipa, chifukwa kuti anati, Yehova ayang'anire pakati pa ine ndi iwe, pamene tisiyana wina ndi mnzake. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201449 ndi Mizipa, chifukwa kuti anati, Yehova ayang'anire pakati pa ine ndi iwe, pamene tisiyana wina ndi mnzake. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa49 Labani adanenanso kuti, “Chauta atiyang'anire ife tonse aŵiri pamene tikulekana. Motero malowo adaŵatcha Mizipa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero49 Unatchedwanso Mizipa, chifukwa iye anati, “Yehova aonetsetsa kuti palibe mmodzi mwa ife adzaswe panganoli ngakhale titatalikirana. Onani mutuwo |