Genesis 31:48 - Buku Lopatulika48 Ndipo Labani anati, Muluwu ndiwo mboni pakati pa ine ndi iwe lero. Chifukwa chake anatcha dzina lake, Galedi; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201448 Ndipo Labani anati, Muluwu ndiwo mboni pakati pa ine ndi iwe lero. Chifukwa chake anatcha dzina lake, Galedi; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa48 Pambuyo pake Labani adati, “Mulu wamiyalawu udzakhala chikumbutso kwa ine ndi iwe.” Nchifukwa chake malowo adaŵatcha Galedi. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero48 Labani anati, “Mulu uwu ndi mboni pakati pa inu ndi ine lero.” Ndi chifukwa chake unatchedwa Galeeda. Onani mutuwo |