Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Genesis 31:47 - Buku Lopatulika

47 Ndipo Labani anatcha pamenepo Yegara-Sahaduta; koma Yakobo anatcha Galedi.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

47 Ndipo Labani anatcha pamenepo Yegara-Sahaduta; koma Yakobo anatcha Galedi.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

47 Tsono muluwo Labani adautcha Yagara-Sahaduta, koma mulu womwewo Yakobe adautcha Galedi.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

47 Labani anawutcha muluwo Yegara-sahaduta, ndipo Yakobo anawutcha Galeeda.

Onani mutuwo Koperani




Genesis 31:47
4 Mawu Ofanana  

Ndipo Yakobo anati kwa abale ake, Sonkhanitsani miyala; ndipo anasonkhanitsa miyala nakundika mulu: ndipo anadya pamulupo.


nafika ku Giliyadi ndi ku dera la Tatimuhodisi; nafika ku Dani-Yaana ndi kuzungulira, kufikira ku Sidoni,


Chifukwa chake ifenso, popeza tizingidwa nao mtambo waukulu wotere wa mboni, titaye cholemetsa chilichonse, ndi tchimoli limangotizinga, ndipo tithamange mwachipiriro makaniwo adatiikira, ndi kupenyerera woyambira ndi womaliza wa chikhulupiriro chathu,


Ndipo ana a Rubeni ndi ana a Gadi analitcha guwa la nsembelo: Ndilo mboni pakati pa ife kuti Yehova ndiye Mulungu.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa