Genesis 31:40 - Buku Lopatulika40 Chotero ndinakhala; usana ludzu linakomola ine, usiku chisanu; tulo tanga tinachoka m'maso mwanga. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201440 Chotero ndinakhala; usana ludzu linakomola ine, usiku chisanu; tulo tanga tinachoka m'maso mwanga. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa40 Nthaŵi zambiri ndinkavutika ndi kutentha masana ndiponso ndi kuzizira usiku. Sindinkatha kuwona tulo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero40 Moyo wanga unali wotere: Dzuwa limanditentha masana ndipo usiku ndimazunzika ndi kuzizira. Tulo sindimalipeza konse. Onani mutuwo |