Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Genesis 31:31 - Buku Lopatulika

31 Ndipo anayankha Yakobo nati kwa Labani, Chifukwa ndinaopa: chifukwa kuti, ndinati, Kapena udzandilanda ine ana ako aakazi.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

31 Ndipo anayankha Yakobo nati kwa Labani, Chifukwa ndinaopa: chifukwa kuti, ndinati, Kapena udzandilanda ine ana ako akazi.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

31 Yakobe adayankha kuti, “Ndinkaopa, chifukwa ndinkaganiza kuti mundilanda ana anuŵa.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

31 Yakobo anayankha Labani kuti, “Ine ndinkaopa chifukwa ndinkaganiza kuti mukhoza kundilanda anawa.

Onani mutuwo Koperani




Genesis 31:31
5 Mawu Ofanana  

Ndipo Abrahamu anati, Chifukwa ndinati, Pompano palibe ndithu kumuopa Mulungu, ndipo adzandipha ine chifukwa cha mkazi wanga.


Tsono ungakhale ukadamuka chifukwa mtima wako ulinkukhumba nyumba ya atate wako, bwanji waba iwe milungu yanga?


Aliyense umpeza ali nayo milungu yako, asakhale ndi moyo: pamaso pa abale athu, tayang'anira zako zili ndi ine, nuzitenge wekha. Pakuti sanadziwe Yakobo kuti Rakele anaiba.


Kuopa anthu kutchera msampha; koma wokhulupirira Yehova adzapulumuka.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa