Genesis 31:26 - Buku Lopatulika26 Ndipo Labani anati kwa Yakobo, Wachitanji? Wathawa kwa ine mobisika ndi kutenga ana anga aakazi, monga mikoli ya lupanga. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201426 Ndipo Labani anati kwa Yakobo, Wachitanji? Wathawa kwa ine mobisika ndi kutenga ana anga akazi, monga mikoli ya lupanga. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa26 Labani adafunsa Yakobe kuti, “Chifukwa chiyani wandinyenga ndi kutenga ana anga aakazi ngati ogwidwa pa nkhondo? Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero26 Tsono Labani anati kwa Yakobo, “Kodi ndakuchita chiyani kuti iwe undinamize ndi kutenga ana anga ngati anthu ogwidwa ku nkhondo? Onani mutuwo |