Genesis 31:21 - Buku Lopatulika21 Ndipo anathawa iye ndi zonse anali nazo: ndipo anauka naoloka panyanja naloza nkhope yake iyang'anire kuphiri la Giliyadi. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201421 Ndipo anathawa iye ndi zonse anali nazo: ndipo anauka naoloka panyanja naloza nkhope yake iyang'anire kuphiri la Giliyadi. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa21 Adatenga zake zonse, nachoka chothaŵa. Adanyamuka, naoloka mtsinje wa Yufurate, nkuyamba ulendo wopita ku dziko lamapiri la Giliyadi. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero21 Choncho anathawa ndi zonse anali nazo. Ananyamuka nawoloka mtsinje wa Yufurate kupita cha ku Giliyadi, dziko la mapiri. Onani mutuwo |