Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Genesis 31:20 - Buku Lopatulika

20 Ndipo Yakobo anathawa kwa Labani Mwaramu mobisika, m'mene sanamuuze iye kuti analinkuthawa.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

20 Ndipo Yakobo anathawa kwa Labani Mwaramu mobisika, m'mene sanamuuze iye kuti analinkuthawa.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

20 Motero Yakobe adampusitsa Labani Mwaramu uja posamuuza kuti akuchoka.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

20 Komanso nthawi iyi nʼkuti Yakobo atamunamiza Labani Mwaramu posamuwuza zoona kuti afuna kuthawa.

Onani mutuwo Koperani




Genesis 31:20
5 Mawu Ofanana  

ndipo Isaki anali wa zaka makumi anai pamene anakwata Rebeka, mwana wamkazi wa Betuele Mwaramu wa ku Padanaramu, mlongo wake wa Labani Mwaramu.


Ndipo Labani ananka kukasenga nkhosa zake: ndipo Rakele anaba aterafi a atate wake.


Ndipo anathawa iye ndi zonse anali nazo: ndipo anauka naoloka panyanja naloza nkhope yake iyang'anire kuphiri la Giliyadi.


Wathawanji iwe mobisika, ndi kundichokera kuseri, osandiuza ine, kuti ndikadakumukitsa iwe ndi kusekerera ndi nyimbo ndi lingaka ndi zeze?


Ndipo muyankhe ndi kuti pamaso pa Yehova Mulungu wanu, Kholo langa ndiye Mwaramu wakuti atayike, natsika kunka ku Ejipito, nagoneragonera komweko ali nao anthu pang'ono, nasandukako mtundu waukulu, wamphamvu, ndi wochuluka anthu ake;


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa