Genesis 31:19 - Buku Lopatulika19 Ndipo Labani ananka kukasenga nkhosa zake: ndipo Rakele anaba aterafi a atate wake. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201419 Ndipo Labani ananka kukasenga nkhosa zake: ndipo Rakele anaba aterafi a atate wake. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa19 Labani anali atapita kokameta nkhosa. Ndipo akadali komweko, Rakele adaba timilungu ta m'nyumba mwa Labani, bambo wake. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero19 Labani atachoka pa khomo kupita kukameta nkhosa, mʼmbuyomu Rakele anaba timafano ta milungu ta abambo ake. Onani mutuwo |