Genesis 31:18 - Buku Lopatulika18 ndipo ananka nazo zoweta zake zonse, ndi chuma chake chonse anachisonkhanitsa, zoweta zake anaziona mu Padanaramu, kuti anke kwa Isaki atate wake ku dziko la Kanani. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201418 ndipo ananka nazo zoweta zake zonse, ndi chuma chake chonse anachisonkhanitsa, zoweta zake anaziona m'Padanaramu, kuti anke kwa Isaki atate wake ku dziko la Kanani. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa18 Ndipo zoŵeta zonse adazitsogoza namazikusa, pamodzi ndi zonse zimene adazipeza ku Mesopotamiya kuja. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero18 anakusa ziweto zake zonse patsogolo natenga katundu wake yense amene anamupeza ku Padanaramu, ndipo ananyamuka kupita ku Kanaani, ku dziko la abambo ake, Isake. Onani mutuwo |