Genesis 31:15 - Buku Lopatulika15 Kodi satiyesa ife alendo? Chifukwa anatigulitsa ife, nathanso kuononga ndalama zathu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201415 Kodi satiyesa ife alendo? Chifukwa anatigulitsa ife, nathanso kuononga ndalama zathu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa15 Ife bambo wathu akutiyesa alendo. Adatigulitsa, ndipo ndalama zomwe adazipezera pa ifezo, adamwaza zonse. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero15 Kodi abambo athu samationa ife ngati alendo? Iwo anatigulitsa ndi kuwononga ndalama zonse anazipeza pa ifezo. Onani mutuwo |