Genesis 29:31 - Buku Lopatulika31 Pamene Yehova anaona kuti anamuda Leya, anatsegula m'mimba mwake; koma Rakele anali wouma. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201431 Pamene Yehova anaona kuti anamuda Leya, anatsegula m'mimba mwake; koma Rakele anali wouma. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa31 Chauta ataona kuti Yakobe sankakonda kwambiri Leya, adalola kuti Leyayo abale ana, koma Rakele ai. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero31 Pamene Mulungu anaona kuti Yakobo sankamukonda Leya kwambiri, Iye analola kuti Leya uja akhale ndi ana, ndi kuti Rakele akhale wosabala. Onani mutuwo |