Genesis 29:30 - Buku Lopatulika30 Ndipo Yakobo analowanso kwa Rakele, namkondanso Rakele kopambana Leya, namtumikira Labani zaka zisanu ndi ziwiri zinanso. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201430 Ndipo Yakobo analowanso kwa Rakele, namkondanso Rakele kopambana Leya, namtumikira Labani zaka zisanu ndi ziwiri zinanso. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa30 Motero Yakobe adaloŵana ndi Rakele, ndipo adamkonda kupambana Leya. Tsono adamgwiriranso ntchito Labani zaka zina zisanu ndi ziŵiri. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero30 Yakobo analowana ndi mkazi wake Rakele, ndipo Yakobo anakonda Rakele kuposa Leya. Ndipo anamugwirira ntchito Labani zaka zina zisanu ndi ziwiri chifukwa cha Rakele. Onani mutuwo |