Genesis 29:29 - Buku Lopatulika29 Ndipo Labani anampatsa mwana wake wamkazi Rakele Biliha mdzakazi wake kuti akhale mdzakazi wa Rakele. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201429 Ndipo Labani anampatsa mwana wake wamkazi Rakele Biliha mdzakazi wake kuti akhale mdzakazi wa Rakele. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa29 (Nthaŵi yomweyo Labani adaperekanso mdzakazi wake Biliha kwa Rakele.) Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero29 Labani anapereka wantchito wake wamkazi Biliha kwa Rakele kuti akhale wantchito wake. Onani mutuwo |