Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Genesis 29:29 - Buku Lopatulika

29 Ndipo Labani anampatsa mwana wake wamkazi Rakele Biliha mdzakazi wake kuti akhale mdzakazi wa Rakele.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

29 Ndipo Labani anampatsa mwana wake wamkazi Rakele Biliha mdzakazi wake kuti akhale mdzakazi wa Rakele.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

29 (Nthaŵi yomweyo Labani adaperekanso mdzakazi wake Biliha kwa Rakele.)

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

29 Labani anapereka wantchito wake wamkazi Biliha kwa Rakele kuti akhale wantchito wake.

Onani mutuwo Koperani




Genesis 29:29
8 Mawu Ofanana  

Ndipo Labani anampatsa mwana wake wamkazi Leya Zilipa mdzakazi wake kuti akhale mdzakazi wa Leya.


Yakobo ndipo anachita chotero namaliza sabata lake; ndipo Labani anampatsa iye Rakele mwana wake wamkazi kuti akwatire iyenso.


Ndipo Yakobo analowanso kwa Rakele, namkondanso Rakele kopambana Leya, namtumikira Labani zaka zisanu ndi ziwiri zinanso.


Ndipo panali pamene Israele anakhala m'dzikomo, Rubeni anamuka nagona ndi Biliha, mkazi wamng'ono wa atate wake: ndipo Israele anamva. Ana aamuna a Yakobo anali khumi ndi awiri:


ana aamuna a Biliha mdzakazi wake wa Rakele: ndiwo Dani ndi Nafutali;


Mibadwo ya Yakobo ndi iyi; Yosefe anali wa zaka khumi ndi zisanu ndi ziwiri analinkudyetsa zoweta pamodzi ndi abale ake; ndipo anali mnyamata pamodzi ndi ana a Biliha, ndi ana aamuna a Zilipa, akazi a atate wake; ndipo Yosefe anamfotokozera atate wake mbiri yao yoipa.


Amenewa ndi ana a Biliha, amene Labani anampatsa Rakele mwana wake wamkazi, amenewo anambalira Yakobo; anthu onse ndiwo asanu ndi awiri.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa