Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Genesis 29:26 - Buku Lopatulika

26 Ndipo Labani anati, Satero kwathu kuno, kupatsa wamng'ono asanapatse wamkulu.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

26 Ndipo Labani anati, Satero kwathu kuno, kupatsa wamng'ono asanapatse wamkulu.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

26 Labani adayankha kuti, “Si mwambo wathu kuno kukwatitsa wamng'ono, mkulu wake asanakwatiwe.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

26 Labani anayankha, “Si mwambo wathu kuno kupereka wamngʼono ku banja, wamkulu asanakwatiwe.

Onani mutuwo Koperani




Genesis 29:26
4 Mawu Ofanana  

Ndipo panali m'mamawa, anaona kuti ndi Leya; ndipo anati kwa Labani, Chiyani wandichitira ine? Kodi sindinakutumikire iwe chifukwa cha Rakele? Wandinyenga ine bwanji?


Umalize sabata lake la uyu, ndipo ndidzakupatsa uyonso chifukwa cha utumiki umene udzanditumikirawo kuonjezera zaka zina zisanu ndi ziwiri.


Ndipo Yosefe anati kwa atate wake, Msatero atate wanga, chifukwa uyu ndi woyamba; ikani dzanja lanu lamanja pamutu wake.


Pakuti muzu wa zoipa zonse ndiwo chikondi cha pa ndalama; chimene ena pochikhumba, anasochera, nataya chikhulupiriro, nadzipyoza ndi zowawa zambiri.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa