Genesis 29:24 - Buku Lopatulika24 Ndipo Labani anampatsa mwana wake wamkazi Leya Zilipa mdzakazi wake kuti akhale mdzakazi wa Leya. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201424 Ndipo Labani anampatsa mwana wake wamkazi Leya Zilipa mdzakazi wake kuti akhale mdzakazi wa Leya. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa24 (Nthaŵi yomweyo Labani adaperekanso mdzakazi wake Zilipa kwa Leya.) Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero24 Ndipo Labani anapereka wantchito wake wamkazi Zilipa kwa Leya kuti akhale wantchito wake. Onani mutuwo |