Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Genesis 29:24 - Buku Lopatulika

24 Ndipo Labani anampatsa mwana wake wamkazi Leya Zilipa mdzakazi wake kuti akhale mdzakazi wa Leya.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

24 Ndipo Labani anampatsa mwana wake wamkazi Leya Zilipa mdzakazi wake kuti akhale mdzakazi wa Leya.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

24 (Nthaŵi yomweyo Labani adaperekanso mdzakazi wake Zilipa kwa Leya.)

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

24 Ndipo Labani anapereka wantchito wake wamkazi Zilipa kwa Leya kuti akhale wantchito wake.

Onani mutuwo Koperani




Genesis 29:24
7 Mawu Ofanana  

Ndipo Sarai mkazi wake wa Abramu sanambalire iye mwana; ndipo anali ndi mdzakazi, wa ku Ejipito, dzina lake Hagara.


Ndipo anamlola Rebeka mlongo wao ndi mlezi wake, amuke pamodzi ndi mnyamata wake wa Abrahamu, ndi anthu ake.


Ndipo panali madzulo Labani anatenga Leya mwana wake wamkazi, nadza naye kwa Yakobo, ndipo iye analowa kwa mkaziyo.


Ndipo panali m'mamawa, anaona kuti ndi Leya; ndipo anati kwa Labani, Chiyani wandichitira ine? Kodi sindinakutumikire iwe chifukwa cha Rakele? Wandinyenga ine bwanji?


ndipo ana aamuna a Zilipa mdzakazi wake wa Leya: ndiwo Gadi ndi Asere: amenewo ndi ana aamuna a Yakobo amene anabala iye mu Padanaramu.


Amenewa ndi ana a Zilipa, amene Labani anampatsa Leya mwana wake wamkazi, amenewo anambalira Yakobo, anthu khumi ndi asanu ndi mmodzi.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa