Genesis 29:23 - Buku Lopatulika23 Ndipo panali madzulo Labani anatenga Leya mwana wake wamkazi, nadza naye kwa Yakobo, ndipo iye analowa kwa mkaziyo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201423 Ndipo panali madzulo Labani anatenga Leya mwana wake wamkazi, nadza naye kwa Yakobo, ndipo iye analowa kwa mkaziyo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa23 Koma usiku umenewo Labani adatenga Leya m'malo mwa Rakele nampatsa Yakobe, ndipo Yakobe adaloŵana ndi Leya. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero23 Koma pokwana usiku, Labani anatenga mwana wake wamkazi Leya namupatsa Yakobo, ndipo Yakobo anagona naye. Onani mutuwo |