Genesis 29:22 - Buku Lopatulika22 Ndipo Labani anasonkhanitsa anthu onse a kumeneko nakonzera madyerero. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201422 Ndipo Labani anasonkhanitsa anthu onse a kumeneko nakonzera madyerero. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa22 Motero Labani adakonza phwando laukwati, naitana anthu onse akumeneko. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero22 Pamenepo Labani anakonza phwando la ukwati, nayitana anthu onse a pamalopo. Onani mutuwo |