Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Genesis 29:22 - Buku Lopatulika

22 Ndipo Labani anasonkhanitsa anthu onse a kumeneko nakonzera madyerero.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

22 Ndipo Labani anasonkhanitsa anthu onse a kumeneko nakonzera madyerero.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

22 Motero Labani adakonza phwando laukwati, naitana anthu onse akumeneko.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

22 Pamenepo Labani anakonza phwando la ukwati, nayitana anthu onse a pamalopo.

Onani mutuwo Koperani




Genesis 29:22
9 Mawu Ofanana  

Ndipo Yakobo anati kwa Labani, Undipatse ine mkazi wanga, chifukwa masiku anga atha, kuti ndilowe kwa iye.


Ndipo panali madzulo Labani anatenga Leya mwana wake wamkazi, nadza naye kwa Yakobo, ndipo iye analowa kwa mkaziyo.


Pamenepo mfumu inawakonzera madyerero akulu ake onse, ndi omtumikira, ndiwo madyerero a Estere; napumulitsa maiko, naninkha zaufulu monga mwa ufulu wa mfumu.


Ndipo ananena ndi ine, Lemba, Odala iwo amene aitanidwa kuphwando la ukwati wa Mwanawankhosa. Ndipo ananena ndi ine, Iwo ndiwo mau oona a Mulungu.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa