Genesis 29:21 - Buku Lopatulika21 Ndipo Yakobo anati kwa Labani, Undipatse ine mkazi wanga, chifukwa masiku anga atha, kuti ndilowe kwa iye. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201421 Ndipo Yakobo anati kwa Labani, Undipatse ine mkazi wanga, chifukwa masiku anga atha, kuti ndilowe kwa iye. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa21 Yakobe adauza Labani kuti, “Tsopano nthaŵi yatha. Patseni mwana wanuyu kuti ndimkwatire.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero21 Kenaka Yakobo anati kwa Labani, “Nthawi yanga ndakwanitsa, ndipatseni mwana wanu kuti ndimukwatire.” Onani mutuwo |