Genesis 29:17 - Buku Lopatulika17 Maso a Leya anali ofooka, koma Rakele anali wokoma thupi ndi wokongola. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201417 Maso a Leya anali ofooka, koma Rakele anali wokoma thupi ndi wokongola. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa17 Leya anali ndi maso ofooka, koma Rakele anali chiphadzuŵa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero17 Leya anali ndi maonekedwe wofowoka koma Rakele anali wa maonekedwe wokongola kwambiri. Onani mutuwo |