Genesis 29:16 - Buku Lopatulika16 Ndipo Labani anali ndi ana aakazi awiri, dzina la wamkulu ndi Leya, dzina la wamng'ono ndi Rakele. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201416 Ndipo Labani anali ndi ana akazi awiri, dzina la wamkulu ndi Leya, dzina la wamng'ono ndi Rakele. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa16 Labani anali ndi ana aakazi aŵiri, wamkulu Leya, wamng'ono Rakele. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero16 Tsono Labani anali ndi ana aakazi awiri; dzina la wamkulu linali Leya, ndipo dzina la wamngʼono linali Rakele. Onani mutuwo |