Genesis 25:28 - Buku Lopatulika28 Ndipo Isaki anakonda Esau, chifukwa anadya nyama yake ya m'thengo; koma Rebeka anakonda Yakobo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201428 Ndipo Isaki anakonda Esau, chifukwa anadya nyama yake ya m'thengo; koma Rebeka anakonda Yakobo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa28 Tsono Isaki ankakonda Esau chifukwa ankadya nyama imene Esauyo ankamupatsa akapha. Koma Rebeka ankakonda Yakobe. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero28 Isake ankakonda Esau chifukwa cha nyama za kutchire zomwe ankakonda kudya, koma Rebeka ankakonda Yakobo. Onani mutuwo |