Genesis 25:27 - Buku Lopatulika27 Ndipo anakula anyamatawo; ndipo Esau anali munthu wakudziwa zakusaka nyama, munthu wa m'thengo; ndipo Yakobo anali munthu wofatsa, wakukhala m'mahema. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201427 Ndipo anakula anyamatawo; ndipo Esau anali munthu wakudziwa zakusaka nyama, munthu wa m'thengo; ndipo Yakobo anali munthu wofatsa, wakukhala m'mahema. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa27 Anyamatawo adakula ndithu, ndipo Esau adasanduka mlenje wodziŵa kusaka nyama, wokonda kuyendayenda. Koma Yakobe anali wachete, wokonda kukhala kunyumba. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero27 Anyamatawo anakula ndipo Esau anakhala katswiri wosaka, munthu wamʼthengo, pamene Yakobo anali munthu wofatsa, wokonda kukhala pa nyumba. Onani mutuwo |