Genesis 25:20 - Buku Lopatulika20 ndipo Isaki anali wa zaka makumi anai pamene anakwata Rebeka, mwana wamkazi wa Betuele Mwaramu wa ku Padanaramu, mlongo wake wa Labani Mwaramu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201420 ndipo Isaki anali wa zaka makumi anai pamene anakwata Rebeka, mwana wamkazi wa Betuele Mwaramu wa ku Padanaramu, mlongo wake wa Labani Mwaramu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa20 ndipo pamene Isaki adakwatira Rebeka mwana wa Betuele Mwaramu wa ku Mesopotamiya, nkuti ali wa zaka makumi anai. Mlongo wa Rebekayo anali Labani, Mwaramu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero20 ndipo Isake anali ndi zaka makumi anayi pamene anakwatira Rebeka mwana wa Betueli Mwaramu wa ku Padanaramu mlongo wa Labani Mwaramu. Onani mutuwo |