Genesis 25:19 - Buku Lopatulika19 Mibadwo ya Isaki mwana wake wa Abrahamu ndi iyi: Abrahamu anabala Isaki: Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201419 Mibadwo ya Isaki mwana wake wa Abrahamu ndi iyi: Abrahamu anabala Isaki: Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa19 Nayi mbiri ya Isaki mwana wa Abrahamu: Abrahamu adabereka Isaki, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero19 Iyi ndi mbiri ya Isake mwana wa Abrahamu. Abrahamu anabereka Isake Onani mutuwo |