Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Genesis 25:19 - Buku Lopatulika

19 Mibadwo ya Isaki mwana wake wa Abrahamu ndi iyi: Abrahamu anabala Isaki:

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

19 Mibadwo ya Isaki mwana wake wa Abrahamu ndi iyi: Abrahamu anabala Isaki:

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

19 Nayi mbiri ya Isaki mwana wa Abrahamu: Abrahamu adabereka Isaki,

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

19 Iyi ndi mbiri ya Isake mwana wa Abrahamu. Abrahamu anabereka Isake

Onani mutuwo Koperani




Genesis 25:19
8 Mawu Ofanana  

Ndipo Abrahamu anamutcha dzina lake la mwana wake wamwamuna amene anabala iye, amene anambalira iye Sara, Isaki.


ndipo Isaki anali wa zaka makumi anai pamene anakwata Rebeka, mwana wamkazi wa Betuele Mwaramu wa ku Padanaramu, mlongo wake wa Labani Mwaramu.


Ana a Abrahamu: Isaki, ndi Ismaele.


Ndi ana a Ketura mkazi wamng'ono wa Abrahamu anabala Zimirani, ndi Yokisani, ndi Medani, ndi Midiyani, ndi Isibaki, ndi Suwa. Ndi ana a Yokisani: Sheba, ndi Dedani.


Ndipo Abrahamu anabala Isaki. Ana a Isaki: Esau, ndi Israele.


Abrahamu anabala Isaki; ndi Isaki anabala Yakobo; ndi Yakobo anabala Yuda ndi abale ake;


mwana wa Yakobo, mwana wa Isaki, mwana wa Abrahamu, mwana wa Tera, mwana wa Nahori,


Ndipo anampatsa iye chipangano cha mdulidwe; ndipo kotero Abrahamu anabala Isaki, namdula tsiku lachisanu ndi chitatu; ndi Isaki anabala Yakobo, ndi Yakobo anabala makolo aakulu aja khumi ndi awiri.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa