Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Genesis 25:17 - Buku Lopatulika

17 Zaka za moyo wa Ismaele ndi izi: zaka zana limodzi kudza makumi atatu ndi zisanu ndi ziwiri: ndipo iye anamwalira, natengedwa akhale ndi a mtundu wake.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

17 Zaka za moyo wa Ismaele ndi izi: zaka zana limodzi kudza makumi atatu ndi zisanu ndi ziwiri: ndipo iye anamwalira, natengedwa akhale ndi a mtundu wake.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

17 (Ismaele anali wa zaka 137 pa nthaŵi imene ankamwalira, ndipo adaikidwa m'manda.)

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

17 Ismaeli anakhala ndi moyo zaka 137. Iye anamwalira ndipo anakakhala ndi anthu a mtundu wake.

Onani mutuwo Koperani




Genesis 25:17
4 Mawu Ofanana  

Ndipo iwe udzanka kwa makolo ako m'mtendere; nudzaikidwa ndi ukalamba wabwino.


Ndipo Abramu anali wa zaka makumi asanu ndi atatu kudza zisanu ndi chimodzi, pamene Hagara anambalira Abramu Ismaele.


Pamene Yakobo anatha kulangiza ana ake aamuna, anafunya mapazi ake pakama, natsirizika, nasonkhanitsidwa kwa anthu a mtundu wake.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa