Genesis 24:33 - Buku Lopatulika33 Ndipo anaika chakudya pamaso pake: koma anati, Sindidzadya ndisananene chimene ndadzera. Ndipo anati, Nenatu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201433 Ndipo anaika chakudya pamaso pake: koma anati, Sindidzadya ndisananene chimene ndadzera. Ndipo anati, Nenatu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa33 Chitabwera chakudya, munthu uja adati, “Sindidya konse mpaka nditanena zimene ndadzera.” Apo Labani adamuuza kuti, “Nenani.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero33 Chakudya chitabwera mlendo uja anati, “Sindidya mpaka nditakuwuzani zimene ndadzera kuno.” Labani anati, “Yankhulani.” Onani mutuwo |