Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Genesis 19:33 - Buku Lopatulika

33 Ndipo anamwetsa atate wao vinyo usiku womwewo; woyamba ndipo analowa nagona naye atate wake; ndipo sanadziwe pomwe anagona ndi pomwe anauka.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

33 Ndipo anamwetsa atate wao vinyo usiku womwewo; woyamba ndipo analowa nagona naye atate wake; ndipo sanadziwe pomwe anagona ndi pomwe anauka.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

33 Choncho usiku womwewo anawo adampatsa vinyo bambo waoyo. Zitatero, mwana wamkuluyo adagona ndi bambo wake. Pamenepo nkuti bamboyo ataledzera kwambiri, kotero kuti sankadziŵa zimene zinkachitika.”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

33 Usiku umenewo analedzeretsa vinyo abambo awo, ndipo wamkuluyo analowa nagona naye. Abambo awo samadziwa kanthu pamene mwanayo anagona naye kapena pamene anadzuka.

Onani mutuwo Koperani




Genesis 19:33
6 Mawu Ofanana  

tiyeni, timwetse atate vinyo, tidzagona naye, kuti tisunge mbeu za atate wathu.


Ndipo panali m'mamawa, woyamba anati kwa wamng'ono, Taona, ndinagona ine ndi atate wanga usiku walero: timwetsenso iye usikunso: udzalowe nugone naye kuti tisunge mbeu za atate wathu.


Vinyo achita chiphwete, chakumwa chaukali chisokosa; wosochera nazo alibe nzeru.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa