Genesis 13:13 - Buku Lopatulika13 Ndipo anthu a ku Sodomu anali oipa ndi ochimwa kwambiri pamaso pa Yehova. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201413 Ndipo anthu a ku Sodomu anali oipa ndi ochimwa kwambiri pamaso pa Yehova. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa13 Anthu amumzindawo anali oipa kwambiri, ndipo ankachimwira Chauta. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero13 Tsono anthu a ku Sodomu anali oyipa ndiponso ankachimwira Yehova kwambiri. Onani mutuwo |