Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Genesis 1:15 - Buku Lopatulika

15 Zikhale zounikira m'thambo la kumwamba, kuti ziunikire padziko lapansi; ndipo kunatero.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

15 Zikhale zounikira m'thambo la kumwamba, kuti ziunikire pa dziko lapansi: ndipo kunatero.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

15 Miyuni imeneyi ikhale ku thambo ndi kumaunikira dziko lapansi,” ndipo zidachitikadi.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

15 zikhale kuthambo kuti ziwunikire pa dziko lapansi. Ndipo zinachitikadi.”

Onani mutuwo Koperani




Genesis 1:15
4 Mawu Ofanana  

Ndipo Mulungu anati, Pakhale zounikira pathambo la kumwamba, zakulekanitsa usana ndi usiku; zikhale zizindikiro ndi nyengo, ndi masiku, ndi zaka;


Ndipo Mulungu anapanga zounikira zazikulu ziwiri; chounikira chachikulu chakulamulira usana, chounikira chaching'ono chakulamulira usiku, ndi nyenyezi zomwe.


Ndipo Mulungu anapanga thambo, nalekanitsa madzi anali pansi pathambolo ndi madzi anali pamwamba pathambolo; ndipo kunatero.


Ichititsa mifunde yonyezimira pambuyo pake; munthu akadati pozama pali ndi imvi.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa