Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Ezara 8:5 - Buku Lopatulika

5 Wa ana a Sekaniya, mwana wa Yahaziele; ndi pamodzi naye amuna mazana atatu.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

5 Wa ana a Sekaniya, mwana wa Yahaziele; ndi pamodzi naye amuna mazana atatu.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

5 Sekaniya, mwana wa Yahaziele, wa fuko la Zatu. Pamodzi ndi iyeyo panali anthu 300.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

5 Sekaniya, mwana wa Yahazieli wa fuko la Zatu. Pamodzi ndi iyeyu panalembedwanso anthu 300.

Onani mutuwo Koperani




Ezara 8:5
3 Mawu Ofanana  

Ndi ana a Hananiya: Pelatiya, ndi Yesaya, ana a Refaya, ana a Arinani, ana a Obadiya, ana a Sekaniya.


Wa ana a Pahatimowabu, Eliehoenai mwana wa Zerahiya; ndi pamodzi naye amuna mazana awiri.


Ndi wa ana a Adini, Ebedi mwana wa Yonatani; ndi pamodzi naye amuna makumi asanu.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa