Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Ezara 8:4 - Buku Lopatulika

4 Wa ana a Pahatimowabu, Eliehoenai mwana wa Zerahiya; ndi pamodzi naye amuna mazana awiri.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

4 Wa ana a Pahatimowabu, Eliehoenai mwana wa Zerahiya; ndi pamodzi naye amuna mazana awiri.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

4 Eliehoenai, mwana wa Zerahiya, wa fuko la Pahatimowabu. Pamodzi ndi iyeyo panali anthu 200.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

4 Elihunai mwana wa Zerahiya, wa fuko la Pahati-Mowabu. Pamodzi ndi iyeyu panalinso anthu ena 400.

Onani mutuwo Koperani




Ezara 8:4
6 Mawu Ofanana  

Ndi a ana a Pahatimowabu: Adina, ndi Kelali, Benaya, Maaseiya, Mataniya, Bezalele, ndi Binuyi, ndi Manase.


Ana a Pahatimowabu, a ana a Yesuwa ndi Yowabu, zikwi ziwiri mphambu mazana asanu ndi atatu kudza khumi ndi awiri.


Wa ana a Sekaniya, wa ana a Parosi, Zekariya; ndi pamodzi naye, powawerenga monga mwa chibadwidwe chao, amuna zana limodzi mphambu makumi asanu.


Wa ana a Sekaniya, mwana wa Yahaziele; ndi pamodzi naye amuna mazana atatu.


Akulu a anthu: Parosi, Pahatimowabu, Elamu, Zatu, Bani,


Ana a Pahatimowabu, a ana a Yesuwa ndi Yowabu, zikwi ziwiri mphambu mazana asanu ndi atatu kudza khumi limodzi ndi asanu ndi atatu.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa