Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Ezara 8:34 - Buku Lopatulika

34 zonsezi anaziwerenga ndi kuziyesa; ndi kulemera kwake konse kunalembedwa nthawi yomweyo.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

34 zonsezi anaziwerenga ndi kuziyesa; ndi kulemera kwake konse kunalembedwa nthawi yomweyo.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

34 Zonsezo adaziŵerenga ndi kuziyesa ndipo adalemba kulemera kwa chinthu chilichonse.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

34 Zonsezi anaziwerenga ndi kuziyeza ndipo analemba kulemera kwa chinthu chilichonse.

Onani mutuwo Koperani




Ezara 8:34
3 Mawu Ofanana  

Mukhale maso ndi kuzisunga mpaka muziyesera pamaso pa ansembe aakulu ndi Alevi, ndi akulu a nyumba za makolo a Israele ku Yerusalemu, m'zipinda za nyumba ya Yehova.


Ndipo pa tsiku lachinai siliva ndi golide ndi zipangizo zinayesedwa m'nyumba ya Mulungu wathu, m'dzanja la Meremoti mwana wa Uriya wansembe, ndi pamodzi naye Eleazara mwana wa Finehasi, ndi pamodzi nao Yozabadi mwana wa Yesuwa, ndi Nowadiya mwana wa Binuyi, Alevi;


Otengedwa ndende, atatuluka m'ndende, anapereka nsembe zopsereza kwa Mulungu wa Israele, ng'ombe khumi ndi ziwiri za Aisraele onse, nkhosa zamphongo makumi asanu ndi anai mphambu zisanu ndi imodzi, anaankhosa makumi asanu ndi awiri mphambu asanu ndi awiri, atonde khumi ndi awiri, akhale nsembe yazolakwa; zonsezi ndizo nsembe yopsereza ya kwa Yehova.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa