Ezara 8:3 - Buku Lopatulika3 Wa ana a Sekaniya, wa ana a Parosi, Zekariya; ndi pamodzi naye, powawerenga monga mwa chibadwidwe chao, amuna zana limodzi mphambu makumi asanu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 Wa ana a Sekaniya, wa ana a Parosi, Zekariya; ndi pamodzi naye, powawerenga monga mwa chibadwidwe chao, amuna zana limodzi mphambu makumi asanu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 Hatusi, mwana wa Sekaniya, wa fuko la Davide. Zekariya, wa fuko la Parosi. Iyeyu adalembedwa pamodzi ndi anthu ena okwanira 150. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 mwana wa Sekaniya wa fuko la Davide; Zekariya wa fuko la Parosi. Pamodzi ndi iyeyu panalembedwa anthu ena 150; Onani mutuwo |