Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Ezara 8:2 - Buku Lopatulika

2 wa ana a Finehasi, Geresomo; wa ana a Itamara, Daniele; wa ana a Davide, Hatusi.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

2 wa ana a Finehasi, Geresomo; wa ana a Itamara, Daniele; wa ana a Davide, Hatusi.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

2 Geresomo, wa fuko la Finehasi. Daniele, wa fuko la Itamara.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

2 Geresomu wa fuko la Finehasi; Danieli wa fuko la Itamara; Hatusi

Onani mutuwo Koperani




Ezara 8:2
6 Mawu Ofanana  

Ana a Davide tsono ombadwira ku Hebroni: woyamba Aminoni wa Ahinowamu wa ku Yezireele, wachiwiri Daniele wa Abigaile wa ku Karimele,


Ndi mwana wa Sekaniya: Semaya; ndi ana a Semaya: Hatusi, ndi Igala, ndi Bariya, ndi Neariya, ndi Safati; asanu ndi mmodzi.


Ndipo akulu a nyumba za makolo ndi awa, ndi chibadwidwe cha iwo okwera nane limodzi kuchokera ku Babiloni, pokhala mfumu Arita-kisereksesi, ndi ichi:


Ndipo ndinawasonkhanitsa ku mtsinje wopita ku Ahava, ndi komweko tinakhala m'misasa masiku atatu; ndipo ndinapenyerera anthu ndi ansembe, koma sindinapezapo wa ana a Levi.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa