Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Ezara 8:12 - Buku Lopatulika

12 Ndi wa ana a Azigadi, Yohanani mwana wa Hakatani; ndi pamodzi naye amuna zana limodzi mphambu khumi limodzi.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

12 Ndi wa ana a Azigadi, Yohanani mwana wa Hakatani; ndi pamodzi naye amuna zana limodzi mphambu khumi limodzi.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

12 Yohanani, mwana wa Hakatani, wa fuko la Azigadi. Pamodzi ndi iyeyo panali anthu 110.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

12 Yohanani, mwana wa Hakatani wa fuko la Azigadi. Pamodzi naye panalinso anthu 110.

Onani mutuwo Koperani




Ezara 8:12
4 Mawu Ofanana  

Ana a Azigadi, chikwi chimodzi mphambu mazana awiri kudza makumi awiri ndi awiri.


Ndi wa ana a Bebai, Zekariya mwana wa Bebai; ndi pamodzi naye amuna makumi awiri mphambu asanu ndi atatu.


Ndi a ana otsiriza a Adonikamu, maina ao ndiwo Elifeleti, Yeiyele, ndi Semaya; ndi pamodzi nao amuna makumi asanu ndi limodzi.


Ana a Azigadi, zikwi ziwiri mphambu mazana atatu kudza makumi awiri ndi awiri.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa