Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Ezara 8:11 - Buku Lopatulika

11 Ndi wa ana a Bebai, Zekariya mwana wa Bebai; ndi pamodzi naye amuna makumi awiri mphambu asanu ndi atatu.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

11 Ndi wa ana a Bebai, Zekariya mwana wa Bebai; ndi pamodzi naye amuna makumi awiri mphambu asanu ndi atatu.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

11 Zekariya, mwana wa Bebai, wa fuko la Bebai. Pamodzi ndi iyeyo panali anthu 28.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

11 Zekariya, mwana wa Bebai wa fuko la Babai. Pamodzi naye analembedwanso anthu 28.

Onani mutuwo Koperani




Ezara 8:11
5 Mawu Ofanana  

Ndi a ana a Bebai: Yehohanani, Hananiya, Zabai, Atilai.


Ana a Bebai, mazana asanu ndi limodzi mphambu makumi awiri kudza awiri.


Ndi wa ana a Selomiti, mwana wa Yosofiya; ndi pamodzi naye amuna zana limodzi mphambu makumi asanu ndi limodzi.


Ndi wa ana a Azigadi, Yohanani mwana wa Hakatani; ndi pamodzi naye amuna zana limodzi mphambu khumi limodzi.


Ana a Bebai, mazana asanu ndi limodzi mphambu makumi awiri kudza asanu ndi atatu.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa