Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Ezara 8:10 - Buku Lopatulika

10 Ndi wa ana a Selomiti, mwana wa Yosofiya; ndi pamodzi naye amuna zana limodzi mphambu makumi asanu ndi limodzi.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

10 Ndi wa ana a Selomiti, mwana wa Yosofiya; ndi pamodzi naye amuna zana limodzi mphambu makumi asanu ndi limodzi.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

10 Selomiti, mwana wa Yosofiya, wa fuko la Bani. Pamodzi ndi iyeyo panali anthu 160.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

10 Selomiti mwana wa Yosifiya wa fuko la Bani. Pamodzi ndi iyeyu panalinso anthu 160.

Onani mutuwo Koperani




Ezara 8:10
2 Mawu Ofanana  

Ndi wa ana a Bebai, Zekariya mwana wa Bebai; ndi pamodzi naye amuna makumi awiri mphambu asanu ndi atatu.


Wa ana a Yowabu, Obadiya mwana wa Yehiyele; ndi pamodzi naye amuna mazana awiri mphambu khumi kudza asanu ndi atatu.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa