Ezara 8:1 - Buku Lopatulika1 Ndipo akulu a nyumba za makolo ndi awa, ndi chibadwidwe cha iwo okwera nane limodzi kuchokera ku Babiloni, pokhala mfumu Arita-kisereksesi, ndi ichi: Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20141 Ndipo akulu a nyumba za makolo ndi awa, ndi chibadwidwe cha iwo okwera nane limodzi kuchokera ku Babiloni, pokhala mfumu Arita-kisereksesi, ndi ichi: Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa1 Nawu mndandanda wa maina a atsogoleri a mabanja amene adabwera nane kuchokera ku Babiloni, pa nthaŵi ya ufumu wa Arita-kisereksesi: Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero1 Nawa mayina a atsogoleri a mabanja amene anabwera nane kuchokera ku Babuloni nthawi ya ulamuliro wa mfumu Aritasasita: Onani mutuwo |