Ezara 7:19 - Buku Lopatulika19 Ndipo zipangizozo akupatsa za utumiki wa nyumba ya Mulungu wako, uzipereka pamaso pa Mulungu wa ku Yerusalemu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201419 Ndipo zipangizozo akupatsa za utumiki wa nyumba ya Mulungu wako, uzipereka pamaso pa Mulungu wa ku Yerusalemu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa19 Ziŵiya zimene akupatsanizi kuti muzitumikira nazo m'Nyumba ya Mulungu wanu, mukazipereke kwa Mulungu ku Yerusalemu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero19 Ziwiya zonse zimene akupatsani kuti mukatumikire nazo mʼNyumba ya Mulungu wanu, kaziperekeni kwa Mulungu ku Yerusalemu. Onani mutuwo |