Ezara 7:18 - Buku Lopatulika18 Ndipo chilichonse chidzakomera iwe ndi abale ako kuchita nazo siliva ndi golide zotsala, ichi muchite monga mwa chifuniro cha Mulungu wanu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201418 Ndipo chilichonse chidzakomera iwe ndi abale ako kuchita nazo siliva ndi golide zotsala, ichi muchite monga mwa chifuniro cha Mulungu wanu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa18 Ndalama zotsala muzigwiritse ntchito monga momwe inuyo ndi abale anu mungafunire malinga nkufuna kwa Mulungu wanu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero18 Ndalama zotsala mudzagwiritse ntchito zimene inuyo ndi abale anu zikakukomerani malingana nʼkufuna kwa Mulungu wanu. Onani mutuwo |