Ezara 7:13 - Buku Lopatulika13 Ndilamulira kuti onse a ana a Israele, ndi ansembe ao, ndi Alevi, mu ufumu wanga, ofuna eni ake kumuka ku Yerusalemu, apite nawe. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201413 Ndilamulira kuti onse a ana a Israele, ndi ansembe ao, ndi Alevi, m'ufumu wanga, ofuna eni ake kumuka ku Yerusalemu, apite nawe. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa13 Tsopano ndikupanga lamulo lakuti Mwisraele aliyense kapena ansembe ao, kapena Alevi okhala m'dziko mwanga, amene afuna kuti apite ku Yerusalemu mwaufulu, apite nawe. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero13 Tsopano ndikulamula kuti Mwisraeli aliyense, wansembe kapena Mlevi wokhala mʼdziko langa, amene akufuna kupita ku Yerusalemu ndi iwe, apite. Onani mutuwo |