Ezara 6:2 - Buku Lopatulika2 Napeza ku Ekibatana m'nyumba ya mfumu m'dera la Mediya, mpukutu, ndi m'menemo munalembedwa motere, chikhale chikumbutso: Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 Napeza ku Ekibatana m'nyumba ya mfumu m'dera la Mediya, mpukutu, ndi m'menemo munalembedwa motere, chikhale chikumbutso: Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 Tsono ku Ekibatana, likulu la dziko la Mediya, kudapezeka mpukutu m'mene mudaalembedwa kuti, “Chikumbutso.” Mau ake anali aŵa: Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 Ndipo ku Ekibatana, likulu la dera la Mediya, kunapezeka mpukutu mmene munalembedwa kuti, Chikumbutso: Onani mutuwo |