Ezara 6:1 - Buku Lopatulika1 Pamenepo analamulira Dariusi mfumu, ndipo anthu anafunafuna m'nyumba ya mabuku mosungira chuma mu Babiloni. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20141 Pamenepo analamulira Dariusi mfumu, ndipo anthu anafunafuna m'nyumba ya mabuku mosungira chuma m'Babiloni. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa1 Atalandira mauwo mfumu Dariusi adapanga lamulo ndipo kafukufuku adachitikadi ku Babiloni m'nyumba mosungira chuma ndi mabuku okhudza mbiri zakale. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero1 Atalandira mawuwo mfumu Dariyo anapereka lamulo ndipo kafukufuku anachitikadi ku Babuloni mʼnyumba yosungira chuma ndi mabuku ambiri yakale. Onani mutuwo |